Nduna ya zofalitsa nkhani yemwenso ndi m’neneri wa boma a Moses Kunkuyu wati kutsegula ofesi ya ukazembe m’dziko la Israel kuthandiza kuthana ndi mavuto omwe achinyamata akhathe kukumana nawo pomwe akugwila ntchito m’dzikoli. A Kunkuyu ayakhula izi pa msokhano wa olemba nkhani ku Lilongwe pomwe mwa zina amatambasula za ulendo wawo wa ku Israel pamodzi […]
Related Articles
This post first appeared on Malawi Nyasa Times - Malawi Breaking News In Malaw, please read the originial post: here